Explore Diverse Views.
Published loading...Updated

Boma lachotsa mlandu wa anthu osokoneza m'dipiti wamtsogoleri Malawi 24 | Latest News from Malawi

Summary by Malawi 24
Boma lalengeza kuti lathetsa mlandu wa anthu atatu omwe anawanjata kamba kosokoneza galimoto zapa m’dipiti wa mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera pomwe ankakakwera ndege ku Chileka mu mzinda wa Blantyre. Omwe amazengedwa mulanduwu ndi a Pearson Chimimba azaka 48, a Lucy Namba azaka 48 komanso a Hector Ndawala azaka 38 zakubadwa. Anthu atatuwa […] The post Boma lachotsa mlandu wa anthu osokoneza m’dipiti wamtsogoleri appeared first on Mal…
DisclaimerThis story is only covered by news sources that have yet to be evaluated by the independent media monitoring agencies we use to assess the quality and reliability of news outlets on our platform. Learn more here.

Bias Distribution

  • There is no tracked Bias information for the sources covering this story.
Factuality

To view factuality data please Upgrade to Premium

Ownership

To view ownership data please Upgrade to Vantage

Malawi 24 broke the news in Malawi on Friday, January 26, 2024.
Sources are mostly out of (0)