Don't Just Read the News, Understand It.
Published loading...Updated

Azipita Chamkakala - a mabungwe Malawi 24 | Latest News from Malawi

Summary by Malawi 24
Atha kuona ma demo angati a Jane Ansah naye Masautso Chamkakala chifukwa a mabungwe ndiye akwiya naye. Ati sakuona phindu lake.  Mabungwe omwe si aboma ati a Chamkala omwe ndi mkulu wa ofesi ya yoyang’anira zozenga milandu m’dziko muno, Director of Prosecutions (DPP), akuyenera kutula pansi udindo polephera kugwira ntchito yake moyenera.  Izi zanenedwa pa […] The post Azipita Chamkakala – a mabungwe appeared first on Malawi 24.
DisclaimerThis story is only covered by news sources that have yet to be evaluated by the independent media monitoring agencies we use to assess the quality and reliability of news outlets on our platform. Learn more here.

Bias Distribution

  • There is no tracked Bias information for the sources covering this story.
Factuality

To view factuality data please Upgrade to Premium

Ownership

To view ownership data please Upgrade to Vantage

Malawi 24 broke the news in Malawi on Thursday, May 9, 2024.
Sources are mostly out of (0)