See the Full Picture.
Published loading...Updated

Boma lauza apolisi kuti amange anthu omwe anazula mipando ku Bingu Malawi 24 | Latest News from Malawi

Summary by Malawi 24
Nduna ya zamasewero Uchizi Mkandawire yapempha apolisi kuti afufuze anthu omwe awononga mipando yoposa 200 ku bwalo la zamasewero la Bingu ku Lilongwe A Mkandawire ayankhula izi atayendera bwalo la zamasewero la Bingu komwe anthu anazula mipando 239 pomwe anakaonela mpira wa pakati pa Silver Strikers ndi Mighty Wanderers. Iwo anati apolisi agwire ntchito yawo […] The post Boma lauza apolisi kuti amange anthu omwe anazula mipando ku Bingu appeare…
DisclaimerThis story is only covered by news sources that have yet to be evaluated by the independent media monitoring agencies we use to assess the quality and reliability of news outlets on our platform. Learn more here.

Bias Distribution

  • There is no tracked Bias information for the sources covering this story.
Factuality

To view factuality data please Upgrade to Premium

Ownership

To view ownership data please Upgrade to Vantage

Malawi 24 broke the news in Malawi on Wednesday, September 27, 2023.
Sources are mostly out of (0)