See the Full Picture.
Published loading...Updated

Yawo ija angoni: fisi wapangidwa ndiwo ku Ntcheu Malawi 24 | Latest News from Malawi

Summary by Malawi 24
Sadyeka uja lero wadyeka: Angoni a ku Ndagoma m’boma la Ntcheu adodometsa gulu pomwe achita ndiwo fisi yemwe wakhala akuwathera mbuzi m’mudzimo. Izi ndi malingana ndi kanema ina yomwe anthu akugawana m’masamba a mchezo yomwe ikuwonetsa azibambo angapo akuwawura fisi yemwe anamupha m’bandakucha wa lolemba pa 2 October. Izi zachitika m’mudzi wa Ndagoma omwe uli […] The post Yawo ija angoni: fisi wapangidwa ndiwo ku Ntcheu appeared first on Malawi
DisclaimerThis story is only covered by news sources that have yet to be evaluated by the independent media monitoring agencies we use to assess the quality and reliability of news outlets on our platform. Learn more here.

Bias Distribution

  • There is no tracked Bias information for the sources covering this story.
Factuality

To view factuality data please Upgrade to Premium

Ownership

To view ownership data please Upgrade to Vantage

Malawi 24 broke the news in Malawi on Monday, October 2, 2023.
Sources are mostly out of (0)